Numeri 34:29 - Buku Lopatulika29 Iwo ndiwo amene Yehova analamulira agawire ana a Israele cholowa chao m'dziko la Kanani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Iwo ndiwo amene Yehova analamulira agawire ana a Israele cholowa chao m'dziko la Kanani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Ameneŵa ndiwo amene Chauta adalamula kuti agaŵe choloŵa cha Aisraele m'dziko la Kanani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Awa ndiwo mayina a anthu amene Yehova analamula kuti agawe cholowa cha Aisraeli mʼdziko la Kanaani. Onani mutuwo |