Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 33:8 - Buku Lopatulika

8 Ndipo anachokera ku Pihahiroti, naoloka pakati pa nyanja nalowa m'chipululu; nayenda ulendo wa masiku atatu m'chipululu cha Etamu, namanga mu Mara.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Ndipo anachokera ku Pihahiroti, naoloka pakati pa nyanja nalowa m'chipululu; nayenda ulendo wa masiku atatu m'chipululu cha Etamu, namanga m'Mara.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Adanyamuka ku Pihahiroti naoloka pakatimpakati pa nyanja, ndipo adaloŵa m'chipululu. Tsono adayenda ulendo wa masiku atatu m'chipululu cha Etamu, nakamanga mahema ku Mara.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Atachoka ku Pihahiroti anadutsa mʼkati mwa nyanja kupita ku chipululu ndipo atayenda masiku atatu mʼchipululu cha Etamu, anamanga misasa yawo ku Mara.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:8
3 Mawu Ofanana  

Lankhula ndi anthu a Israele, kuti abwerere m'mbuyo nagone patsogolo pa Pihahiroti, pakati pa Migidoli ndi nyanja, patsogolo pa Baala-Zefoni; pandunji pake mugone panyanja.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa