Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 33:30 - Buku Lopatulika

30 Nachokera ku Hasimona, nayenda namanga mu Meseroti.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Nachokera ku Hasimona, nayenda namanga m'Meseroti.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Adanyamuka ku Hasimona, nakamanga mahema ao ku Meseroti.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Atachoka ku Hasimona anakamanga ku Moseroti.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 33:30
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Mose anavula Aroni zovala zake, naveka Eleazara mwana wake; ndipo Aroni anafa pomwepo pamwamba paphiri. Pamenepo Mose ndi Eleazara anatsika m'phirimo.


Nachokera ku Mitika, nayenda namanga mu Hasimona.


Nachokera ku Meseroti, nayenda namanga mu Bene-Yaakani.


nufe m'phiri m'mene ukweramo, nuitanidwe kunka kwa anthu a mtundu wako; monga Aroni mbale wako anafa m'phiri la Hori, naitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wake;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa