Numeri 33:20 - Buku Lopatulika20 Nachokera ku Rimoni-Perezi, nayenda namanga mu Libina. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Nachokera ku Rimoni-Perezi, nayenda namanga m'Libina. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Adanyamuka ku Rimoni-Perezi, nakamanga mahema ao ku Libina. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Atachoka ku Rimoni-Perezi anakamanga ku Libina. Onani mutuwo |