Numeri 31:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo zakunkhondo, zotsalira zofunkha zonse adazifunkha ankhondowa, ndizo nkhosa zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu zikwi makumi asanu ndi awiri kudza zisanu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo zakunkhondo, zotsalira zofunkha zonse adazifunkha ankhondowa, ndizo nkhosa zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu zikwi makumi asanu ndi awiri kudza zisanu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Zofunkha zotsala zimene ankhondowo adalanda zinali izi: nkhosa 675,000, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Zotsala pa zolanda ku nkhondo zimene ankhondowo anatenga zinali nkhosa 675,000, Onani mutuwo |