Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:31 - Buku Lopatulika

31 Ndipo Mose ndi Eleazara wansembe anachita monga Yehova anamuuza Mose.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Ndipo Mose ndi Eleazara wansembe anachita monga Yehova anamuuza Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Tsono Mose ndi wansembe Eleazara adachitadi zomwe Chauta adalamula Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Ndipo Mose ndi wansembe Eliezara anachita monga Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:31
4 Mawu Ofanana  

mwana wa Abisuwa mwana wa Finehasi, mwana wa Eleazara, mwana wa Aroni wansembe wamkulu.


Ndipo anthu anawerama, nalambira. Ndipo ana a Israele anamuka nachita monga Yehova adalamulira Mose ndi Aroni; anachita momwemo.


Ndipo ku gawo la ana a Israele utenge munthu mmodzi mwa anthu makumi asanu, mwa ng'ombe, mwa abulu, mwa nkhosa ndi mbuzi, mwa zoweta zonse, momwemo; nuzipereke kwa Alevi, akusunga udikiro wa chihema cha Yehova.


Ndipo zakunkhondo, zotsalira zofunkha zonse adazifunkha ankhondowa, ndizo nkhosa zikwi mazana asanu ndi limodzi mphambu zikwi makumi asanu ndi awiri kudza zisanu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa