Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 31:26 - Buku Lopatulika

26 Werengani zakunkhondo, ndizo anthu, ndi zoweta, iwe, ndi Eleazara wansembe, ndi akulu a nyumba za makolo za khamulo;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Werengani zakunkhondo, ndizo anthu, ndi zoweta, iwe, ndi Eleazara wansembe, ndi akulu a nyumba za makolo za khamulo;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 “Iwe, ndi wansembe Eleazara, pamodzi ndi atsogoleri a mabanja a mpingo, muŵerenge zofunkha zimene adalanda pa nkhondo, anthu pamodzi ndi nyama zomwe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 “Iwe ndi wansembe Eliezara ndiponso akuluakulu a mabanja a anthuwa, muwerenge anthu onse ndi ziweto zomwe zinagwidwa ku nkhondo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 31:26
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


nugawe zakunkhondo pawiri; pakati pa othira nkhondo amene anatuluka kunkhondo, ndi khamu lonse.


Koma ng'ombe ndi zofunkha za mzinda uwu Israele anadzifunkhira monga mwa mau a Yehova amene analamulira Yoswa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa