Numeri 3:3 - Buku Lopatulika3 Awa ndi maina a ana aamuna a Aroni, ansembe odzozedwawo, amene anawadzaza manja ao achite ntchito ya nsembe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Awa ndi maina a ana amuna a Aroni, ansembe odzozedwawo, amene anawadzaza manja ao achite ntchito ya nsembe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ameneŵa ndiwo maina a ana a Aroni, ansembe odzozedwa amene iye adaŵasankha kuti azitumikira pa ntchito yaunsembe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Amenewa ndi mayina a ana aamuna a Aaroni, ansembe odzozedwa omwe anapatulidwa kuti azitumikira ngati ansembe. Onani mutuwo |