Numeri 29:32 - Buku Lopatulika32 Ndi tsiku lachisanu ndi chiwiri ng'ombe zisanu ndi ziwiri, nkhosa zamphongo ziwiri, anaankhosa khumi ndi anai, a chaka chimodzi, opanda chilema; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndi tsiku lachisanu ndi chiwiri ng'ombe zisanu ndi ziwiri, nkhosa zamphongo ziwiri, anaankhosa khumi ndi anai, a chaka chimodzi, opanda chilema; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 “Pa tsiku lachisanu ndi chiŵiri mupereke ng'ombe zisanu ndi ziŵiri zamphongo, nkhosa ziŵiri zamphongo, anaankhosa khumi ndi anai amphongo a chaka chimodzi opanda chilema. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 “ ‘Pa tsiku lachisanu ndi chiwiri muzipereka ngʼombe zazimuna zisanu ndi ziwiri, nkhosa zazimuna ziwiri ndi ana ankhosa amuna khumi ndi anayi a chaka chimodzi, zonse zopanda chilema. Onani mutuwo |