Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 29:15 - Buku Lopatulika

15 ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo nao anaankhosa khumi ndi anai;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 ndi limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo nao anaankhosa khumi ndi anai;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 ndi wa kilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Pa mwana wankhosa aliyense mwa ana ankhosa aamuna khumi ndi anayiwo, muzipereka chakudya cha kilogalamu imodzi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 29:15
2 Mawu Ofanana  

ndi nsembe yake yaufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, atatu a magawo khumi akhale a efa wa ng'ombe imodzi, momwemo nazo ng'ombe khumi ndi zitatuzo, awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo imodzi, momwemo nazo nkhosa zamphongo ziwirizo;


ndi tonde mmodzi akhale nsembe yauchimo; pamodzi ndi nsembe yopsereza yosalekeza, nsembe yake yaufa, ndi nsembe yake yothira.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa