Numeri 28:7 - Buku Lopatulika7 Ndi nsembe yake yothira ya mwanawankhosa mmodziyo ndiyo limodzi la magawo anai la hini; m'malo opatulika uthirire Yehova nsembe yothira ya chakumwa cholimba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndi nsembe yake yothira ya mwanawankhosa mmodziyo ndiyo limodzi la magawo anai la hini; m'malo opatulika uthirire Yehova nsembe yothira ya chakumwa cholimba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Chopereka cha chakumwa pa nkhosa iliyonse chikhale yokwanira lita limodzi. Muzithira vinyo waukaliyo m'malo opatulika, kuchipereka kwa Chauta. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Chopereka chachakumwa chikhale lita imodzi yachakumwa chaukali pa nkhosa iliyonse. Muzithira pamalo opatulika, kupereka kwa Yehova. Onani mutuwo |