Numeri 28:4 - Buku Lopatulika4 Mwanawankhosa mmodziyo umpereke m'mawa, ndi mwanawankhosa winayo umpereke madzulo; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mwanawankhosa mmodziyo umpereke m'mawa, ndi mwanawankhosa winayo umpereke madzulo; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mwanawankhosa mmodzi muzimpereka m'maŵa, winayo muzimpereka madzulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Mmawa muzipereka mwana wankhosa mmodzi ndipo winayo madzulo. Onani mutuwo |