Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 28:29 - Buku Lopatulika

29 limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

29 limodzi la magawo khumi likhale la mwanawankhosa mmodzi, momwemo ndi anaankhosa asanu ndi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

29 ndiponso wa kilogaramu limodzi pa mwanawankhosa aliyense.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

29 Ndipo pa mwana wankhosa aliyense mwa asanu ndi awiri aja, kilogalamu imodzi.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 28:29
2 Mawu Ofanana  

ndi nsembe yake ya efa wa ufa wosalala wosakaniza ndi mafuta, atatu a magawo khumi akhale a ng'ombe imodzi, awiri a magawo khumi akhale a nkhosa yamphongo imodzi,


tonde mmodzi wakutetezera inu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa