Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 28:18 - Buku Lopatulika

18 Tsiku loyamba pali kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Tsiku loyamba pali kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 Pa tsiku loyamba pazikhala msonkhano wopatulika. Musagwire ntchito yotopetsa,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Pa tsiku loyamba muzichita msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 28:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo tsiku loyamba kukhale kusonkhana kopatulika, ndi tsiku lachisanu ndi chiwiri kukhalenso kusonkhana kopatulika; pasachitike ntchito masikuwo, zokhazi zakudya anthu onse ndizo muzichita.


Ndipo tsiku lachisanu ndi chiwiri mukhale nako kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena.


Momwemonso tsiku la zipatso zoyamba, pobwera nayo nsembe ya ufa watsopano kwa Yehova, m'chikondwerero chanu cha Masabata, muzikhala nako kusonkhana kopatulika; musamachita ntchito ya masiku ena.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa