Numeri 27:13 - Buku Lopatulika13 Utaliona iwenso udzaitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wako, monga anaitanidwa Aroni mbale wako; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Utaliona iwenso udzaitanidwa kunka kwa anthu a mtundu wako, monga anaitanidwa Aroni mbale wako; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndipo utaliwona, udzamwalira monga momwe adachitira Aroni mbale wako, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ukakaliona udzamwalira ngati Aaroni mʼbale wako, Onani mutuwo |