Numeri 26:3 - Buku Lopatulika3 Pamenepo Mose ndi Eleazara wansembe ananena nao m'zidikha za Mowabu pa Yordani kufupi ku Yeriko, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pamenepo Mose ndi Eleazara wansembe ananena nao m'zidikha za Mowabu pa Yordani kufupi ku Yeriko, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Tsono Mose ndi wansembe Eleazara adalankhula ndi atsogoleri m'zigwa za ku Mowabu, pafupi ndi mtsinje wa Yordani ku Yeriko, adati, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Kotero mu zigwa za Mowabu pafupi ndi mtsinje wa Yorodani ku Yeriko, Mose ndi wansembe Eliezara anayankhula nawo kuti, Onani mutuwo |