Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 25:17 - Buku Lopatulika

17 Sautsa Amidiyani ndi kuwakantha;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Sautsa Amidiyani ndi kuwakantha;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 “Uŵathire nkhondo Amidiyani, ndiponso uŵaononge

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 “Amidiyani ndi adani anu ndipo uwaphe,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 25:17
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Mowabu anati kwa akulu a Midiyani, Tsopano msonkhano uwu udzanyambita zonse zili pozinga pathu, monga ng'ombe zinyambita msipu wa kubusa. Ndipo Balaki mwana wa Zipori anali mfumu ya Mowabu masiku amenewo.


Ndipo Israele anakhala mu Sitimu, ndipo anthu anayamba kuchita chigololo ndi ana aakazi a Mowabu;


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, ndi kuti,


popeza akusautsani ndi manyengo ao amene anakunyengani nao; m'chija cha Peori, ndi cha Kozibi, mwana wamkazi wa kalonga wa ku Midiyani, mlongo wao, amene adamupha tsiku la mliri, m'chija cha Peori.


Muubwezere, monganso uwu unabwezera, ndipo muwirikize kawiri, monga mwa ntchito zake; m'chikhomo unathiramo, muuthirire chowirikiza.


Koma ana a Israele anachita choipa pamaso pa Yehova; ndipo Yehova anawapereka m'dzanja la Midiyani zaka zisanu ndi ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa