Numeri 24:8 - Buku Lopatulika8 Mulungu amtulutsa mu Ejipito; ali nayo mphamvu yonga ya njati; adzawadya amitundu, ndiwo adani ake. Nadzamphwanya mafupa ao, ndi kuwapyoza ndi mivi yake. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Mulungu amtulutsa m'Ejipito; ali nayo mphamvu yonga ya njati; adzawadya amitundu, ndiwo adani ake. Nadzamphwanya mafupa ao, ndi kuwapyoza ndi mivi yake. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mulungu adaŵatulutsa m'dziko la Ejipito. Ali ndi mphamvu zonga za njati, adzapha mitundu ya adani ao, adzaswa mafupa ao ndi kuŵaboola ndi mivi yao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Mulungu womutulutsa mʼdziko la Igupto ali ndi mphamvu ngati za njati. Amawononga mitundu yomuwukira ndi kuphwanya mafupa awo, amalasa ndi mivi yake. Onani mutuwo |