Numeri 24:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Balamu anakweza maso ake, naona Israele alikukhala monga mwa mafuko ao; ndipo mzimu wa Mulungu unadza pa iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Balamu anakweza maso ake, naona Israele alikukhala monga mwa mafuko ao; ndipo mzimu wa Mulungu unadza pa iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Adaona Aisraele ali m'mahema mwao, fuko lililonse pa lokha. Tsono mzimu wa Mulungu udatsika pa iye, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Balaamu atayangʼana, anaona Aisraeli atamanga misasa yawo fuko ndi fuko. Pamenepo mzimu wa Mulungu unabwera pa iye Onani mutuwo |