Numeri 23:15 - Buku Lopatulika15 Ndipo anati kwa Balaki, Imani pano pa nsembe yopsereza yanu, ndipite ine ndikakomane ndi Iye uko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Ndipo anati kwa Balaki, Imani pano pa nsembe yopsereza yanu, ndipite ine ndikakomane ndi Iye uko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Balamu adauza Balaki kuti, “Imani pano pafupi ndi nsembe yanu yopsereza, ine ndipite ndikakumane ndi Chauta apo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Balaamu anawuza Balaki kuti, “Khalani pano pafupi ndi nsembe yanu pamene ine ndikukakumana ndi Mulungu cha uko.” Onani mutuwo |