Numeri 23:13 - Buku Lopatulika13 Ndipo Balaki anati naye, Tiyetu, upite nane kumalo kwina, kumene ukawaona; udzaona malekezero ao okha, osawaona onse; ndipo pokhala pamenepo ukanditembererere iwo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndipo Balaki anati naye, Tiyetu, upite nane kumalo kwina, kumene ukawaona; udzaona malekezero ao okha, osawaona onse; ndipo pokhala pamenepo ukanditembererere iwo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Balaki adamuuzanso kuti, “Tiyeni tipite limodzi ku malo ena kumene mungathe kuŵaona Aisraelewo. Mukangoona okhawo amene ayandikira pafupi, koma simukaona onse. Tsono muŵatemberere m'malo mwanga, mutaima pamenepo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kenaka Balaki anawuza Balaamu kuti, “Tiye tipite limodzi ku malo ena komwe ungawaone. Udzangoona gulu limodzi osati onsewo. Ndipo pamenepo, ukawatemberere mʼmalo mwanga.” Onani mutuwo |