Numeri 22:34 - Buku Lopatulika34 Pamenepo Balamu anati kwa mthenga wa Yehova, Ndachimwa, popeza sindinadziwe kuti munaima mondiletsa m'njira; ndipo tsopano, ngati chikuipirani, ndibwerera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Pamenepo Balamu anati kwa mthenga wa Yehova, Ndachimwa, popeza sindinadziwa kuti munaima mondiletsa m'njira; ndipo tsopano, ngati chikuipirani, ndibwerera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Balamu adayankha mngelo wa Chauta uja kuti, “Ndachimwa. Sindinalikudziŵa kuti mukunditsekera njira. Nchifukwa chake tsono, ngati zakuipirani, ndibwerera.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Balaamu anati kwa mngelo wa Yehova uja, “Ndachimwa. Sindinadziwe kuti munayima pa njira kunditsutsa. Tsopano ngati Inu simunakondwe, ineyo ndibwerera.” Onani mutuwo |