Numeri 22:29 - Buku Lopatulika29 Pamenepo Balamu anati kwa bulu, Chifukwa wandipeputsa; mukadakhala lupanga m'dzanja langa tsopano, ndikadakupha iwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Pamenepo Balamu anati kwa bulu, Chifukwa wandipeputsa; mukadakhala lupanga m'dzanja langa tsopano, ndikadakupha iwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Balamu adauza buluyo kuti, “Chifukwa choti ukuseŵera nane, ndikadakhala ndi lupanga m'manja mwanga, ndikadakupha.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 Balaamu anati kwa buluyo, “Wandipusitsa, ndikanakhala ndi lupanga mʼmanja mwanga, ndikanakupha pomwe pano.” Onani mutuwo |