Numeri 22:19 - Buku Lopatulika19 Ndikupemphani, tsono, khalani pano inu usiku uno womwe; kuti ndidziwe chomwe Yehova adzanenanso nane. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndikupemphani, tsono, khalani pano inu usiku uno womwe; kuti ndidziwe chomwe Yehova adzanenanso nane. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndiye inu tsono, gonani konkuno usiku uno, monga adachitira anzanu aja, kuti ndidziŵe ngati pali zina zimene Chauta andiwuze.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Tsopano mukhale kuno usiku uno monga ena anachitira, ndidzaona chimene Yehova adzandiwuza.” Onani mutuwo |