Numeri 21:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo Israele analonjeza chowinda kwa Yehova, nati, Mukadzaperekatu anthu awa m'dzanja langa, ndidzaononga mizinda yao konse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo Israele analonjeza chowinda kwa Yehova, nati, Mukadzaperekatu anthu awa m'dzanja langa, ndidzaononga midzi yao konse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono Aisraele adalumbira kwa Chauta kuti, “Ngati muŵapereka anthu ameneŵa m'manja mwathu, ife tidzaonongeratu mizinda yao.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo Israeli anachita lonjezo ili kwa Yehova: “Mukapereka anthu awa mʼdzanja lathu ife tidzawonongeratu mizinda yawo.” Onani mutuwo |