Numeri 20:4 - Buku Lopatulika4 Mwalowa nao bwanji msonkhano wa Yehova m'chipululu muno, kuti tifere mommuno, ife ndi zoweta zathu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mwalowa nao bwanji msonkhano wa Yehova m'chipululu muno, kuti tifere mommuno, ife ndi zoweta zathu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Chifukwa chiyani mwafikitsa mpingo wa Chauta kuchipululu kuno, kuti ife tifere kuno pamodzi ndi zoŵeta zathu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Chifukwa chiyani unabweretsa gulu la Yehova mʼchipululu muno, kuti ife ndi ziweto zathu tife kuno? Onani mutuwo |