Numeri 20:29 - Buku Lopatulika29 Pamene khamu lonse linaona kuti Aroni adamwalira, anamlira Aroni masiku makumi atatu, ndiyo mbumba yonse ya Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201429 Pamene khamu lonse linaona kuti Aroni adamwalira, anamlira Aroni masiku makumi atatu, ndiyo mbumba yonse ya Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa29 Pamene mpingo udamva kuti Aroni wamwalira, mpingo wonse wa Israele udalira maliro a Aroni masiku makumi atatu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero29 ndipo pamene anthu onse anamva kuti Aaroni wafa, nyumba yonse ya Israeli inamulira Aaroniyo masiku makumi atatu. Onani mutuwo |