Numeri 20:18 - Buku Lopatulika18 Koma Edomu ananena naye, Usapitire pakati pa ine, kuti ndingatuluke kukomana nawe ndi lupanga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Koma Edomu ananena naye, Usapitire pakati pa ine, kuti ndingatuluke kukomana nawe ndi lupanga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Koma Edomu adayankha kuti, “Musadzere kuno, kuti ndingafike kudzakubayani ndi lupanga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Koma Edomu anayankha kuti, “Musadutse kuno: Mukangoyesera tidzabwera ndi kumenyana nanu ndi lupanga.” Onani mutuwo |