Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:23 - Buku Lopatulika

23 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 ndipo ankhondo ake ngokwanira 35,400.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 35,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:23
5 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Benjamini, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai.


Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni.


Owerengedwa onse a chigono cha Efuremu ndiwo zikwi makumi khumi mphambu zisanu ndi zitatu kudza zana limodzi, monga mwa makamu ao. Iwo ndiwo aziyenda gulu lachitatu paulendo.


Iwo ndiwo ana a Benjamini monga mwa mabanja ao; ndipo owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi.


Ndipo anawerenga ana a Benjamini a m'mizinda tsiku lija amuna zikwi makumi awiri mphambu zisanu ndi chimodzi akusolola lupanga; osawerenga okhala mu Gibea, ndiwo amuna osankhika mazana asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa