Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 2:23 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 35,400.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

23 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu zisanu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 ndipo ankhondo ake ngokwanira 35,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:23
5 Mawu Ofanana  

Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Benjamini chinali 35,400.


Lotsatira lidzakhala fuko la Benjamini. Mtsogoleri wa Abenjamini ndi Abidani mwana wa Gideoni.


Anthu onse aamuna mu msasa wa Efereimu, chiwerengero chawo ndi 108,100 monga mwa magulu awo. Iwowo azikhala achitatu posamuka.


Awa ndiwo anali mabanja a Benjamini. Amene nawerengedwa analipo 45,600.


Tsiku limenelo Abenjamini anasonkhanitsa kuchokera ku mizinda yawo ankhondo 26,000 amalupanga awo, osawerengera anthu ena 700 a ku Gibeya amene anasankhidwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa