Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 19:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni:

Onani mutuwo Koperani




Numeri 19:1
2 Mawu Ofanana  

Ndipo simudzasenzapo uchimo, mutakwezako zokometsetsa zake; ndipo musamaipsa zinthu zopatulika za ana a Israele, kuti mungafe.


Ili ndi lemba la chilamulo Yehova adalamulirachi, ndi kuti, Nena ndi ana a Israele kuti azikutengera ng'ombe yaikazi yofiira, yangwiro yopanda chilema, yosamanga m'goli;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa