Numeri 18:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo asunge udikiro wako, ndi udikiro wa chihema chonse; koma asayandikize zipangizo za malo opatulika, ndi guwa la nsembe, kuti mungafe, iwo ndi inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo asunge udikiro wako, ndi udikiro wa chihema chonse; koma asayandikize zipangizo za malo opatulika, ndi guwa la nsembe, kuti mungafe, iwo ndi inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Iwowo adzakutumikirani ndi kugwiranso ntchito zonse zam'chihema. Koma asadzafike pafupi ndi zipangizo za m'malo opatulika kapena guwa, kuti iwowo pamodzi ndi inuyo mungafe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Iwowo azikutumikirani ndipo azichita ntchito zonse za ku tenti, koma asamafike pafupi ndi zipangizo za ku malo opatulika kapena guwa lansembe, kuopa kuti iwo ndi inu mungafe. Onani mutuwo |