Numeri 18:22 - Buku Lopatulika22 Ndipo kuyambira tsopano ana a Israele asayandikize chihema chokomanako, angamasenze uchimo kuti angafe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Ndipo kuyambira tsopano ana a Israele asayandikize chihema chokomanako, angamasenze uchimo kuti angafe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Kuyambira tsopano Aisraele asamafika pafupi ndi chihema chamsonkhano, kuti angachimwe ndipo angafe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kuyambira tsopano mpaka mʼtsogolo Aisraeli asamapite pafupi ndi tenti ya msonkhano. Ngati atero adzasenza zotsatira za tchimo lawo ndipo adzafa. Onani mutuwo |