Numeri 16:21 - Buku Lopatulika21 Dzipatuleni pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Dzipatuleni pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 “Chokani pakati pa mpingowu kuti ndiwononge onse nthaŵi imodzi.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 “Chokani pakati pa gulu ili kuti ndithetse mkanganowu kamodzinʼkamodzi.” Onani mutuwo |