Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 16:20 - Buku Lopatulika

20 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Ndipo Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Yehova anawuza Mose ndi Aaroni kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:20
3 Mawu Ofanana  

Koma nyumba ya Israele inapandukira Ine m'chipululu, sanayende m'malemba anga, nanyoza maweruzo anga, amene munthu akawachita adzakhala nao ndi moyo; ndi masabata anga anawaipsa kwambiri; pamenepo ndidati ndiwatsanulire ukali wanga m'chipululu kuwatha.


Ndipo Kora anasonkhanitsa khamu lonse mopikisana nao ku khomo la chihema chokomanako; ndipo ulemerero wa Yehova unaoneka kwa khamu lonse.


Dzipatuleni pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa