Numeri 16:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Mose anatuma kukaitaniza Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu; koma anati, Sitifikako: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Mose anatuma kukaitaniza Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu; koma anati, Sitifikako: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Apo Mose adatuma munthu kukaitana Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu. Ndipo iwo adati, “Ife sitibwera kumeneko. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Kenaka Mose anayitana Datani ndi Abiramu, ana aamuna a Eliabu koma iwo anati, “Sitibwera! Onani mutuwo |