Numeri 14:19 - Buku Lopatulika19 Khululukiranitu mphulupulu ya anthu awa, monga mwa chifundo chanu chachikulu, ndi monga mudalekerera anthu awa, kuyambira Ejipito kufikira tsopano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Khululukiranitu mphulupulu ya anthu awa, monga mwa chifundo chanu chachikulu, ndi monga mudalekerera anthu awa, kuyambira Ejipito kufikira tsopano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Ndikukupemphani kuti muŵakhululukire kuchimwa kwao anthu ameneŵa kaamba ka chifundo chanu chachikulu ndi chosasinthika, ndiponso chifukwa mwakhala mukuŵakhululukira anthu ameneŵa kuyambira ku Ejipito mpaka tsopano lino.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Chifukwa cha kukula kwa chikondi chanu chosasinthika, akhululukireni anthuwa tchimo lawo monga mwakhala mukuwakhululukira kuchokera pa nthawi imene anachoka ku Igupto mpaka tsopano.” Onani mutuwo |