Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 13:9 - Buku Lopatulika

9 Wa fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Wa fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 M'fuko la Benjamini, adatuma Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 kuchokera ku fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:9
6 Mawu Ofanana  

Wa fuko la Zebuloni, Gadiele mwana wa Sodi.


Wa fuko la Efuremu, Hoseya mwana wa Nuni.


Khalani amphamvu, limbikani mitima, musamachita mantha, kapena kuopsedwa chifukwa cha iwowa; popeza Yehova Mulungu wanu ndiye amene amuka nanu; Iye sadzakusowani, kapena kukusiyani.


Ndipo Yehova, Iye ndiye amene akutsogolera; Iye adzakhala ndi iwe, Iye sadzakusowa kapena kukusiya; usamachita mantha, usamatenga nkhawa.


Musamawaopa; mukumbukire bwino chimene Yehova Mulungu wanu anachitira Farao, ndi Ejipito wonse;


Musamaopa pamaso pao; popeza Yehova Mulungu wanu ali pakati pa inu, Mulungu wamkulu ndi woopsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa