Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 13:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 kuchokera ku fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Wa fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Wa fuko la Benjamini, Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 M'fuko la Benjamini, adatuma Paliti mwana wa Rafu.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:9
6 Mawu Ofanana  

kuchokera ku fuko la Zebuloni, Gadieli mwana wa Sodi;


kuchokera ku fuko la Efereimu, Hoseya mwana wa Nuni;


Khalani amphamvu ndi olimba mtima. Musachite nawo mantha kapena kunjenjemera pamaso pawo, chifukwa Yehova Mulungu wanu apita nanu. Sadzakusiyani kapena kukutayani.”


Yehova mwini ndiye akukutsogolerani ndipo adzakhala nanu. Sadzakusiyani kapena kukutayani. Usachite mantha ndiponso usataye mtima.”


Koma musachite nawo mantha, kumbukirani bwino zimene Yehova Mulungu wanu anachita ndi Farao pamodzi ndi Igupto yense.


Musaopsedwe nawo pakuti Yehova Mulungu wanu, amene ali pakati panu, ndi Mulungu wamkulu ndi woopsa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa