Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 13:6 - Buku Lopatulika

6 Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 M'fuko la Yuda, adatuma Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 kuchokera ku fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune;

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:6
16 Mawu Ofanana  

Ndi ana a Kalebe mwana wa Yefune: Iru, Ela, ndi Naamu; ndi ana a Ela, ndi Kenazi.


Koma Kalebe anatontholetsa anthu pamaso pa Mose, nati, Tikwere ndithu ndi kulilandira lathulathu; popeza tikhozadi kuchita kumene.


Wa fuko la Simeoni, Safati mwana wa Hori.


Wa fuko la Isakara, Igala mwana wa Yosefe.


koma mtumiki wanga Kalebe, popeza anali nao mzimu wina, nanditsata monsemo, ndidzamlowetsa iyeyu m'dziko muja analowamo; ndi mbeu zake zidzakhala nalo.


simudzalowa inu m'dzikolo, ndinakwezapo dzanja langa kukukhalitsani m'mwemo, koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni ndiwo.


Koma Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, anakhala ndi moyo mwa amuna aja adamukawo kukazonda dziko.


Ndipo Yoswa mwana wa Nuni, ndi Kalebe mwana wa Yefune, ndiwo a iwo aja adazonda dzikolo, anang'amba zovala zao;


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Maina a amunawo ndiwo: wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa