Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 13:6 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

6 kuchokera ku fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune;

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

6 Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

6 Wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

6 M'fuko la Yuda, adatuma Kalebe mwana wa Yefune.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:6
16 Mawu Ofanana  

Ana a Kalebe mwana wa Yefune anali awa: Iru, Ela ndi Naama. Mwana wa Ela anali Kenazi.


Koma Kalebe anawakhalitsa chete anthuwo pamaso pa Mose, ndipo anati, “Tiyeni tipite ndithu ndi kutenga dzikolo, pakuti tingathe kulitenga.”


kuchokera ku fuko la Simeoni, Safati mwana wa Hori;


kuchokera ku fuko la Isakara, Igala mwana wa Yosefe;


Koma mtumiki wanga Kalebe, pakuti ali ndi mtima wosiyana ndi ena ndiponso amanditsatira ndi mtima wonse, ndidzamulowetsa mʼdziko limene anapitamolo ndipo zidzukulu zake zidzalandira dzikolo ngati cholowa chawo.


Palibe ndi mmodzi yemwe mwa inu amene adzalowe mʼdziko lomwe ndinalumbira mokweza manja kuti likhale lanu, kupatula Kalebe mwana wa Yefune ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Mwa anthu amene anakaona dzikolo, Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune ndi okhawo amene anapulumuka.


Yoswa mwana wa Nuni ndi Kalebe mwana wa Yefune, omwe anali amodzi mwa amene anakazonda nawo dziko, anangʼamba zovala zawo


Chifukwa Yehova anali atawuza Aisraeliwo kuti adzafera ndithu mʼchipululu, ndipo palibe ndi mmodzi yemwe amene anatsala kupatula Kalebe mwana wa Yefune ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Mayina awo ndi awa: Kalebe mwana wa Yefune, wochokera ku fuko la Yuda,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa