Numeri 13:33 - Buku Lopatulika33 Tinaonakonso Anefili, ana a Anaki, obadwa ndi Anefili; ndipo tinaoneka m'maso mwathu ngati ziwala; momwemonso tinaoneka m'maso mwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Tinaonakonso Anefili, ana a Anaki, obadwa ndi Anefili; ndipo tinaoneka m'maso mwathu ngati ziwala; momwemonso tinaoneka m'maso mwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Tidaonanso ziphona, (zidzukulu za Aanaki). Ifeyo tinkaoneka ngati ziwala, ndipo iwonso ankatiwona ngati ziwala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Kumeneko tinaona Anefili (ana a Aanaki ochokera kwa Nefili). Ifeyo timangodziona ngati ziwala mʼmaso mwawo, ndipo kwa iwo timaonekadi motero ndithu.” Onani mutuwo |