Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 12:9 - Buku Lopatulika

9 Pamenepo Yehova anawapsera mtima iwo; nawachokera Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Pamenepo Yehova anawapsera mtima iwo; nawachokera Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pamenepo Chauta adaŵakwiyira, nachokapo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Ndipo Yehova anawakwiyira, nachoka.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 12:9
5 Mawu Ofanana  

Ndipo analeka kunena naye, ndipo Mulungu anakwera kuchokera kwa Abrahamu.


Ndipo Yehova anapita atatha kunena naye Abrahamu: ndipo Abrahamu anabwera kumalo kwake.


Ndidzamuka ndi kubwerera kunka kumalo kwanga, mpaka adzavomereza kupalamula kwao, nafunafuna nkhope yanga; m'msauko mwao adzandifunafuna mwachangu.


Ndipo anthu anaipa, namadandaula m'makutu a Yehova; ndipo pamene Yehova anamva anapsa mtima; ndi moto wa Yehova unayaka pakati pao, nunyeketsa ku chilekezero cha chigono.


Ndipo Mose anamva anthu alikulira m'mabanja ao, yense pakhomo pa hema wake; ndipo Yehova anapsa mtima ndithu, ndipo kudamuipira Mose.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa