Numeri 12:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anati, Kodi Yehova wanena ndi Mose yekha? Sananenanso ndi ife nanga? Ndipo Yehova anamva. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anati, Kodi Yehova wanena ndi Mose yekha? Sananenanso ndi ife nanga? Ndipo Yehova anamva. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Iwowo adafunsa kuti, “Kodi nzoona kuti Chauta adalankhula kudzera mwa Mose yekha? Kodi sadalankhulenso kudzera mwa ife?” Chauta adazimva zimenezo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Iwowo anafunsa kuti, “Kodi Yehova anayankhula kudzera mwa Mose yekha? Kodi sanayankhule kudzeranso mwa ife?” Ndipo Yehova anamva zimenezi. Onani mutuwo |