Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 11:34 - Buku Lopatulika

34 Ndipo anatcha malowo dzina lake Kibroti-Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

34 Ndipo anatcha malowo dzina lake Kibroti-Hatava; popeza pamenepo anaika anthu osusuka.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

34 Nchifukwa chake malowo adaŵatcha Mandaankhuli, chifukwa choti kumeneko ndiko kumene adakwirira anthu ankhuli.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

34 Nʼchifukwa chake malowo anawatcha Kibiroti Hatava chifukwa pamenepo anakwirirapo anthu osusuka aja.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:34
6 Mawu Ofanana  

pamenepo mkwiyo wa Mulungu unawaukira, ndipo anapha mwa onenepa ao, nagwetsa osankhika a Israele.


Kuchokera ku Kibroti-Hatava anthuwo anayenda kunka ku Hazeroti; nakhala ku Hazeroti.


Nachokera ku chipululu cha Sinai, nayenda namanga mu Kibroti-Hatava.


Nachokera ku Kibroti-Hatava, nayenda namanga mu Hazeroti.


Koma zinthu izi zinachitika, zikhale zotichenjeza ife, kuti tisalakalake zoipa ife, monganso iwowo analakalaka.


Ku Tabera, ndi ku Masa, ndi ku Kibroti-Hatava, munautsanso mkwiyo wa Yehova.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa