Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 11:30 - Buku Lopatulika

30 Ndipo Mose ndi akulu onse a Israele anasonkhana kuchigono.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Ndipo Mose ndi akulu onse a Israele anasonkhana kuchigono.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Tsono Mose ndi atsogoleri a Aisraele aja adabwerera ku mahema.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Mose ndi akuluakulu a Israeli aja anabwerera ku msasa.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:30
3 Mawu Ofanana  

Koma Mose anati kwa iye, Kodi uchita nsanje nao chifukwa cha ine? Mwenzi anthu onse a Yehova atakhala aneneri? Mwenzi Yehova atawaikira mzimu wake!


Ndipo kudachokera mphepo kwa Yehova, n'kudza nazo zinziri zochokera kunyanja, ndipo zidagwa kuchigono, ulendo wa tsiku limodzi dera lino, ndi ulendo wa tsiku limodzi dera lina, pozungulira pa chigono, ndipo zinabisa nthaka ngati muyeso wa mikono iwiri.


Ndipo Mose anauka namuka kwa Datani ndi Abiramu; ndi akulu a Israele anamtsata.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa