Numeri 11:27 - Buku Lopatulika27 Ndipo anathamanga anyamata, nauza Mose, nati, Elidadi ndi Medadi alikunenera m'chigono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201427 Ndipo anathamanga anyamata, nauza Mose, nati, Elidadi ndi Medadi alikunenera m'chigono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa27 Ndiye mnyamata wina adathamanga nakauza Mose kuti, “Elidadi ndi Meladi akulosa kumahemaku.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero27 Mnyamata wina anathamanga kudzawuza Mose kuti, “Elidadi ndi Medadi akunenera mu msasa.” Onani mutuwo |