Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 11:19 - Buku Lopatulika

19 Simudzadya tsiku limodzi, kapena masiku awiri, kapena masiku asanu, kapena masiku khumi, kapena masiku makumi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Simudzadya tsiku limodzi, kapena masiku awiri, kapena masiku asanu, kapena masiku khumi, kapena masiku makumi awiri;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Simudzaidya tsiku limodzi lokha, kapena masiku aŵiri okha, kapena masiku asanu okha, kapena masiku khumi okha, kapena masiku makumi aŵiri okha ai.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Simudzadya tsiku limodzi lokha, kapena masiku awiri, kapena asanu, khumi kapena masiku makumi awiri,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:19
3 Mawu Ofanana  

Potero anadya nakhuta kwambiri; ndipo anawapatsa chokhumba iwo.


Ndipo unene ndi anthu, Mudzipatuliretu, mawa mudzadya nyama; popeza mwalira m'makutu a Yehova, ndi kuti, Adzatipatsa nyama ndani? Popeza tinakhala bwino mu Ejipito. Potero Yehova adzakupatsani nyama, ndipo mudzadya.


koma mwezi wamphumphu, kufikira ibwera m'mphuno mwako, ndi kuti ufukidwa nayo, pakuti mwakaniza Yehova wakukhala pakati pa inu, ndi kulira pamaso pake, ndi kuti, Tinatulukiranji mu Ejipito?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa