Numeri 10:34 - Buku Lopatulika34 Ndipo mtambo wa Yehova unali pamwamba pao msana, pakuyenda iwo kuchokera kuchigono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Ndipo mtambo wa Yehova unali pamwamba pao msana, pakuyenda iwo kuchokera kuchigono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Mtambo wa Chauta unkaŵaphimba masana, nthaŵi iliyonse pamene ankanyamuka pamahemapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Mtambo wa Yehova unkawaphimba masana pamene ankasamuka pa misasa yawo. Onani mutuwo |