Numeri 10:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Chauta adauza Mose kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova anawuza Mose kuti, Onani mutuwo |
napenya, ndi kuona mfumu inaima pa nsanamira yake polowera; ndi atsogoleri, ndi malipenga, anali kwa mfumu; ndi anthu onse a m'dziko anakondwera, naomba amalipenga; oimbira omwe analiko ndi zoimbirazo, nalangiza poimbira cholemekeza. Pamenepo Ataliya anang'amba zovala zake, nati, Chiwembu, chiwembu.